Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 8:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Tsopano Elisa anauza mayi amene anamuukitsira mwana uja,+ kuti: “Nyamuka, iwe ndi banja lako, ukakhale monga mlendo kulikonse kumene ungakakhale,+ chifukwa Yehova abweretsa njala.+ Njalayo idzatenga zaka 7.”+

  • 2 Mafumu 8:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Gehazi akufotokozera mfumuyo mmene Elisa anaukitsira munthu wakufa,+ anangomva mayi wa mwana amene anaukitsidwayo akudandaulira mfumu kuti imupatse nyumba yake ndi munda wake.+ Nthawi yomweyo Gehazi anati: “Mbuye wanga+ mfumu, mayiyo ndi uyu, ndiponso mwana wake amene Elisa anamuukitsa uja ndi uyu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena