Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 12:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tsopano m’dzikomo munagwa njala, ndipo Abulamu ananyamuka kulowera ku Iguputo kukakhala kumeneko monga mlendo.+ Anatero chifukwa njalayo inafika poipa kwambiri m’dzikomo.+

  • Genesis 26:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Tsopano m’dzikomo munagwanso njala, kuwonjezera pa njala yoyamba ija imene inagwa m’masiku a Abulahamu.+ Choncho Isaki anapita kwa Abimeleki, mfumu ya Afilisiti, ku Gerari.+

  • Genesis 47:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Kenako anauza Farao kuti: “Tabwera kuno kudzakhala monga alendo,+ chifukwa akapolo anufe tilibe chakudya chopatsa ziwetozi,+ popeza njala yafika poipa kwambiri ku Kanani.+ Ndiye chonde, tiloleni ife akapolo anu tikhale ku Goseni.”+

  • Rute 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Tsopano zinachitika kuti, m’masiku amene oweruza+ anali atsogoleri, m’dzikomo munagwa njala.+ Ndiyeno munthu wina anasamuka ku Betelehemu+ wa ku Yuda kukakhala m’dziko la Mowabu+ monga mlendo. Anasamuka ndi mkazi wake ndi ana ake awiri aamuna.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena