Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 37:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Amidiyani aja anakagulitsa Yosefe ku Iguputo kwa Potifara. Potifara anali nduna ya panyumba ya Farao,+ ndiponso anali mkulu wa asilikali olondera mfumu.+

  • 1 Samueli 8:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Idzatenganso gawo limodzi mwa magawo 10+ a zokolola za m’minda yanu ya mbewu ndi ya mpesa, n’kuzipereka kwa nduna za panyumba ya mfumu+ ndi kwa antchito ake.

  • 2 Mafumu 8:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndiyeno mfumuyo inapempha mayiyo kuti aifotokozere nkhani yonse,+ ndipo mayiyo anafotokozadi. Kenako mfumuyo inauza nduna ya panyumba yake+ kuti: “Mayiyu um’bwezere zinthu zake zonse, ndipo umupatse ndalama zimene akanapeza pa zokolola za kumunda kwake pa nthawi yonse imene anachokapo kufikira lero.”+

  • Esitere 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pa tsiku la 7, pamene mtima wa mfumu unali kukondwera ndi vinyo,+ mfumu inauza Mehumani, Bizita, Haribona,+ Bigita, Abagata, Zetara ndi Karikasi, nduna 7 za panyumba ya mfumu zimene zinali kutumikira+ Mfumu Ahasiwero,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena