Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 14:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Patapita nthawi ana a Isiraeli anadutsa pakati pa nyanja, panthaka youma,+ madziwo ataima ngati khoma* kudzanja lawo lamanja ndi lamanzere.+

  • Yoswa 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ansembe onyamula likasa la pangano la Yehova anangoima chilili panthaka youma+ pakati pa mtsinje wa Yorodano. Anaimabe choncho pamene Aisiraeli onse anali kuwoloka panthaka youmayo,+ kufikira mtundu wonse unatha kuwoloka mtsinje wa Yorodano.

  • 2 Mafumu 2:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ali pamenepo, anatenga chovala chauneneri cha Eliya chimene chinagwa chija n’kumenya nacho madzi a mtsinjewo,+ n’kunena kuti: “Ali kuti Yehova Mulungu wa Eliya?”+ Atamenya madziwo, pang’onopang’ono madziwo anagawanika uku ndi uku, ndipo Elisa anawoloka.

  • Salimo 114:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Kodi chinavuta n’chiyani nyanja iwe kuti uthawe?+

      Kodi iwe Yorodano chinavuta n’chiyani kuti ubwerere m’mbuyo?+

  • Yesaya 11:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yehova adzaphwetsa chigawo cha nyanja ya Iguputo,+ ndipo adzayendetsa dzanja lake moopseza Mtsinje*+ pogwiritsa ntchito mpweya wake wotentha. Adzamenya mtsinjewo pokwapula timitsinje take 7, ndipo adzachititsa anthu kuwolokapo nsapato zili kuphazi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena