Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 22:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Azipereke kwa ogwira ntchito+ osankhidwa a m’nyumba ya Yehova, kuti akazipereke kwa amene akugwira ntchitoyo m’nyumba ya Yehova, kuti amate ming’alu ya nyumbayo.+

  • 2 Mbiri 24:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mfumuyo ndi Yehoyada ankapereka ndalamazo kwa anthu ogwira ntchito+ yokonza nyumba ya Yehova.+ Iwowo analemba ntchito anthu osema miyala+ ndi amisiri+ okonza nyumba ya Yehova.+ Analembanso ntchito amisiri a mkuwa ndi a zitsulo oti akonze nyumba ya Yehova.+

  • 2 Mbiri 34:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kenako anapereka ndalamazo m’manja mwa ogwira ntchito osankhidwa a m’nyumba ya Yehova.+ Ndiyeno iwowa anapereka ndalamazo kwa anthu amene anali kugwira ntchito m’nyumba ya Yehova, omwe anazigwiritsa ntchito yokonzera nyumbayo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena