5 Azipereke kwa ogwira ntchito+ osankhidwa a m’nyumba ya Yehova, kuti akazipereke kwa amene akugwira ntchitoyo m’nyumba ya Yehova, kuti amate ming’alu ya nyumbayo.+
12 Mfumuyo ndi Yehoyada ankapereka ndalamazo kwa anthu ogwira ntchito+ yokonza nyumba ya Yehova.+ Iwowo analemba ntchito anthu osema miyala+ ndi amisiri+ okonza nyumba ya Yehova.+ Analembanso ntchito amisiri a mkuwa ndi a zitsulo oti akonze nyumba ya Yehova.+