Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 4:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pakuti ndi mtundu winanso uti wamphamvu+ umene milungu yake ili pafupi nawo, monga mmene Yehova Mulungu wathu alili pafupi ndi ife, tikamaitanira pa iye+ nthawi zonse?

  • Deuteronomo 33:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Isiraeli adzakhala motetezeka,+

      Kasupe wa Yakobo adzakhala mosatekeseka,+

      M’dziko lokhala ndi chakudya ndi vinyo watsopano.+

      Ndipo kumwamba kwake kudzagwetsa mame.+

  • Salimo 147:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Sanachite zimenezi ndi mtundu wina uliwonse,+

      Ndipo mitundu inayo sikudziwa zigamulo zake.+

      Tamandani Ya, anthu inu!+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena