Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 5:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Chotero anatumiza uthenga ndi kusonkhanitsa olamulira onse ogwirizana a Afilisiti ku Asidodi ndi kuwauza kuti: “Tichite nalo chiyani likasa la Mulungu wa Isiraeli?” Pamapeto pake iwo anati: “Likasa limeneli la Mulungu wa Isiraeli tilitumize kumzinda wa Gati.”+ Choncho anapititsa likasa la Mulungu wa Isiraeli kumeneko atayenda nalo mozungulira.

  • 1 Samueli 27:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Patapita nthawi, uthenga unafika kwa Sauli wonena kuti Davide anathawira ku Gati. Atamva zimenezo sanapitenso kukam’sakasaka.+

  • 2 Samueli 1:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Anthu inu musanene zimenezi mumzinda wa Gati.+

      Musalengeze zimenezi m’misewu ya Asikeloni,+

      Kuopera kuti ana aakazi a Afilisiti angasangalale,+

      Kuopera kuti ana aakazi a anthu osadulidwa angakondwere.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena