Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 16:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pajatu maso a Yehova+ akuyendayenda padziko lonse lapansi+ kuti aonetse mphamvu zake kwa anthu amene mtima wawo+ uli wathunthu kwa iye. Mwachita zopusa+ pankhani imeneyi, chifukwa kuyambira tsopano anthu azichita nanu nkhondo.”+

  • Salimo 18:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Mulungu woona Ndiye amandilimbitsa,*+

      Ndipo adzasalaza njira yanga.+

  • Salimo 28:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Yehova ndiye mphamvu kwa anthu ake,+

      Iye ndi malo achitetezo odzetsa chipulumutso chachikulu kwa wodzozedwa wake.+

  • Yesaya 40:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Iye amapereka mphamvu kwa munthu wotopa,+ ndipo wofooka amam’patsa nyonga zochuluka.+

  • 1 Petulo 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ngati wina akulankhula, alankhule monga mwa mawu opatulika+ a Mulungu. Ngati wina akutumikira,+ atumikire modalira mphamvu imene Mulungu amapereka,+ kuti m’zinthu zonse Mulungu alemekezeke+ kudzera mwa Yesu Khristu. Ulemerero+ ndi mphamvu, ndi zake mpaka muyaya. Ame.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena