Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 30:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Aroni azipaka ena mwa magazi a nyama ya nsembe yamachimo yophimbira machimo,+ panyanga za guwalo kuti aziphimbira machimo. Azichita zimenezi kamodzi pa chaka+ m’mibadwo yanu yonse. Kwa Yehova, guwalo ndi lopatulika koposa.”

  • 2 Mbiri 29:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Tsopano ansembe anazipha n’kuzipereka nsembe yamachimo pamodzi ndi magazi ake paguwa lansembe kuti aphimbe machimo a Aisiraeli onse,+ popeza mfumu inati nsembe yopsereza ndi yamachimoyo+ ikhale ya Aisiraeli onse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena