-
2 Mafumu 9:27Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
27 Ahaziya+ mfumu ya Yuda, anaona zonsezo moti anayamba kuthawa kudzera njira ya kumunda.*+ (Pambuyo pake Yehu anayamba kum’tsatira, ndipo anati: “Ameneyonso m’kantheni!” Choncho anam’kanthadi ali m’galeta lake pamene anali kuthawira ku Guru, kufupi ndi ku Ibuleamu.+ Iye anapitirizabe kuthawa mpaka ku Megido+ kumene anakafera.+
-