Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 7:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pa nthawi yonse imene ndinali kuyendayenda pakati pa ana a Isiraeli onse,+ kodi ndinalankhulapo mawu ndi limodzi mwa mafuko onse a Isiraeli,+ fuko limene ndinalilamula kutsogolera anthu anga Aisiraeli, kuti, ‘N’chifukwa chiyani anthu inu simunandimangire nyumba ya mitengo ya mkungudza?’”’

  • Salimo 78:71
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 71 Anamutenga kumene anali kuweta nkhosa zoyamwitsa,+

      Anamutenga kuti akhale m’busa wa ana a Yakobo amene ndi anthu ake,+

      Ndi Isiraeli, amene ndi cholowa chake.+

  • Yohane 10:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ine ndine m’busa wabwino.+ M’busa wabwino amataya moyo wake chifukwa cha nkhosa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena