Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nyimbo ya Solomo 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Inu ana aakazi a ku Yerusalemu,+ ine ndine mtsikana wakuda ngati mahema a ku Kedara,+ koma wokongola ngati nsalu za mahema+ a Solomo.

  • Yesaya 21:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Anthu otsala pa amuna oponya mivi ndi uta, omwe ndi amuna amphamvu a ana a Kedara, adzakhala ochepa,+ pakuti Yehova Mulungu wa Isiraeli wanena zimenezi.”+

  • Ezekieli 27:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Unalemba ntchito Aluya+ ndi atsogoleri onse a ku Kedara+ kuti azikugulitsira malonda. Iwo anali kukugulitsira ana a nkhosa amphongo, nkhosa zamphongo ndi mbuzi zamphongo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena