Genesis 35:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Atatero anachoka, ndipo anthu a m’mizinda yowazungulira anagwidwa ndi mantha ochokera kwa Mulungu,+ moti sanatsatire ana a Yakobo kuti akawathire nkhondo. 2 Mbiri 14:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Kuwonjezera apo, anawononga mizinda yonse yozungulira Gerari chifukwa mantha+ ochokera kwa Yehova anagwira anthu a m’mizindayo. Iwo anafunkha mizinda yonseyo, chifukwa munali zambiri zoti afunkhe.+ 2 Mbiri 17:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Mantha+ ochokera kwa Yehova anagwira maufumu onse a m’mayiko ozungulira Yuda, ndipo sanachite nkhondo ndi Yehosafati.+
5 Atatero anachoka, ndipo anthu a m’mizinda yowazungulira anagwidwa ndi mantha ochokera kwa Mulungu,+ moti sanatsatire ana a Yakobo kuti akawathire nkhondo.
14 Kuwonjezera apo, anawononga mizinda yonse yozungulira Gerari chifukwa mantha+ ochokera kwa Yehova anagwira anthu a m’mizindayo. Iwo anafunkha mizinda yonseyo, chifukwa munali zambiri zoti afunkhe.+
10 Mantha+ ochokera kwa Yehova anagwira maufumu onse a m’mayiko ozungulira Yuda, ndipo sanachite nkhondo ndi Yehosafati.+