Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Anthu adzamva+ ndipo adzatekeseka.+

      Okhala ku Filisitiya adzamva zopweteka ngati za pobereka.+

  • Deuteronomo 33:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Palibe wina wofanana ndi Mulungu woona+ wa Yesuruni,+

      Amene amayenda m’mlengalenga pokuthandiza,+

      Amene amayenda pamitambo mu ulemerero wake.+

  • Yoswa 9:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Iwo anamuyankha kuti: “Akapolo anufe tachokera kudziko lakutali kwambiri.+ Tabwera chifukwa tamva za dzina+ la Mulungu wanu, Yehova. Tamva mbiri yake ndi zonse zimene anachita ku Iguputo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena