-
2 Mbiri 25:23Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
23 Yehoasi mfumu ya Isiraeli anagwira+ Amaziya mfumu ya Yuda, mwana wa Yehoasi, mwana wa Yehoahazi ku Beti-semesiko. Kenako Yehoasi anatenga Amaziya n’kupita naye ku Yerusalemu,+ ndipo anakagumula mpanda wa Yerusalemu kuyambira pa Chipata cha Efuraimu+ mpaka kukafika pa Chipata cha Pakona.+ Anagumula mpata waukulu mikono 400.
-