Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 23:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Panalinso alonda 4,000 a pachipata+ ndi anthu 4,000 oimbira Yehova zitamando+ ndi zoimbira+ zimene Davide anati, “Zimenezi ndazipanga kuti tizitamandira Mulungu.”

  • Salimo 150:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Mutamandeni mwa kuliza lipenga la nyanga ya nkhosa.+

      Mutamandeni ndi choimbira cha zingwe ndi zeze.+

  • Yesaya 38:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Inu Yehova bwerani mudzandipulumutse,+ ndipo tidzaimba nyimbo zimene ine ndinapeka. Ndidzaimba ndi zoimbira za zingwe+

      Kunyumba ya Yehova masiku onse a moyo wathu.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena