Yoswa 16:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Ana a Yosefe,+ omwe ndi Manase ndi Efuraimu,+ analandira gawo lawo.+ 2 Mbiri 17:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Iye anaika magulu ankhondo m’mizinda yonse ya Yuda yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri. Anamanganso midzi ya asilikali m’dziko la Yuda ndi m’mizinda ya Efuraimu imene Asa bambo ake analanda.+ 2 Mbiri 34:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Komanso, m’mizinda ya Manase,+ Efuraimu,+ Simiyoni, mpaka Nafitali, ndi m’malo onse owonongedwa ozungulira mizindayi, Hoseya 11:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 “Kodi ndikusiyirenji iwe Efuraimu?+ Kodi ndikuperekerenji kwa adani iwe Isiraeli?+ Kodi ndikusandutsirenji ngati Adima?+ Kodi ndikuchitirenji zofanana ndi zimene ndinachitira Zeboyimu?+ Mtima wanga wasintha+ ndipo pa nthawi imodzimodziyo wadzaza ndi chisoni.
2 Iye anaika magulu ankhondo m’mizinda yonse ya Yuda yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri. Anamanganso midzi ya asilikali m’dziko la Yuda ndi m’mizinda ya Efuraimu imene Asa bambo ake analanda.+
6 Komanso, m’mizinda ya Manase,+ Efuraimu,+ Simiyoni, mpaka Nafitali, ndi m’malo onse owonongedwa ozungulira mizindayi,
8 “Kodi ndikusiyirenji iwe Efuraimu?+ Kodi ndikuperekerenji kwa adani iwe Isiraeli?+ Kodi ndikusandutsirenji ngati Adima?+ Kodi ndikuchitirenji zofanana ndi zimene ndinachitira Zeboyimu?+ Mtima wanga wasintha+ ndipo pa nthawi imodzimodziyo wadzaza ndi chisoni.