Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 20:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Yesaya anayankha kuti: “Chizindikiro+ chochokera kwa Yehova, chakuti Yehova adzakwaniritsadi mawu amene walankhula, ndi ichi: Kodi mthunzi uyende masitepe 10 kupita kutsogolo, kapena uyende masitepe 10 kubwerera m’mbuyo pamasitepe olowera m’nyumba?”

  • 2 Mbiri 32:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Ndiyeno zinachitika kuti pamene akalonga a ku Babulo+ anatumiza nthumwi zawo kwa iye,+ kuti zikam’funse za chizindikiro cholosera zam’tsogolo+ chimene chinachitika m’dzikolo, Mulungu woona anamusiya+ kuti amuyese+ ndi kuona zonse zimene zinali mumtima mwake.+

  • Yesaya 38:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndichititsa mthunzi wa dzuwa+ umene wapita kale kutsogolo pamasitepe a Ahazi, kuti ubwerere m’mbuyo masitepe 10.”’”+ Choncho dzuwa linabwerera m’mbuyo pang’onopang’ono masitepe 10 pa masitepe pomwe linali litapita kale kutsogolo.+

  • Yesaya 38:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Pa nthawiyi, Hezekiya anati: “Kodi chizindikiro chakuti ndidzapita kunyumba ya Yehova n’chiyani?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena