Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 11:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiyeno ku chiyambi kwa chaka,+ pa nthawi imene mafumu anali kupita kukamenya nkhondo,+ Davide anatumiza Yowabu, atumiki ake ndi Isiraeli yense kuti akawononge ana a Amoni+ ndi kuzungulira mzinda wa Raba.+ Koma Davide anatsalira ku Yerusalemu.

  • 1 Mafumu 20:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Pambuyo pake mneneri uja+ anapita kwa mfumu ya Isiraeli n’kuiuza kuti: “Pitani, kalimbitseni gulu lanu lankhondo+ ndi kuganizira zomwe mudzachite,+ popeza kumayambiriro kwa chaka chamawa mfumu ya Siriya ija idzabweranso kudzamenyana nanu.”+

  • 2 Mafumu 13:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Pambuyo pa zimenezi Elisa anamwalira ndipo anamuika m’manda.+ Tsopano panali magulu a achifwamba+ achimowabu+ amene ankabwera m’dzikolo kumayambiriro kwa chaka chilichonse.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena