Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 taona, ndichita mogwirizanadi ndi mawu ako.+ Ndithu ndikupatsa mtima wanzeru ndi womvetsa zinthu+ moti ndi kale lonse sipanakhalepo munthu ngati iwe, ndipo pambuyo pako sipadzakhalanso wina ngati iwe.+

  • Salimo 34:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mikango yamphamvu ingakhale ndi chakudya chochepa ndipo ingamve njala.+

      Koma ofunafuna Yehova sadzasowa chilichonse chabwino.+

  • Aefeso 3:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Tsopano kwa iye amene angathe kuchita zazikulu kwambiri kuposa zonse zimene timapempha kapena kuganiza,+ malinga ndi mphamvu yake imene ikugwira ntchito+ mwa ife,

  • 1 Yohane 5:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Komanso, popeza timadziwa kuti amatimvera tikapempha chilichonse,+ timakhala ndi chikhulupiriro kuti tilandira zinthu zimene tamupemphazo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena