Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 10:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Golide+ amene ankabwera kwa Solomo chaka chimodzi, anali wolemera matalente 666,*+

  • 2 Mbiri 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mfumuyo inachititsa kuti ku Yerusalemu siliva ndi golide akhale wochuluka kwambiri ngati miyala,+ ndiponso kuti matabwa a mkungudza akhale ochuluka kwambiri ngati mitengo yamkuyu+ ya ku Sefela.+

  • Salimo 68:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Chifukwa cha kachisi wanu yemwe ali ku Yerusalemu,+

      Mafumu adzabweretsa mphatso kwa inu.+

  • Salimo 72:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Iye akhale ndi moyo wautali,+ ndipo apatsidwe wina mwa golide wa ku Sheba.+

      Nthawi zonse anthu azimupempherera.

      Adalitsike tsiku lililonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena