Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 21:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Mfumuyo inakupemphani moyo. Ndipo munaipatsadi,+

      Munaipatsa masiku ochuluka kuti ikhale mpaka kalekale, ndithu mpaka muyaya.+

  • Yohane 14:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Kwatsala kanthawi pang’ono ndipo dziko silidzandionanso.+ Koma inu mudzandiona,+ chifukwa ndili ndi moyo, inunso mudzakhala ndi moyo.+

  • 1 Yohane 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 (Ife taona ndipo tikuchitira umboni+ ndi kunena kwa inu za moyo wosatha+ umene unachokera kwa Atate ndipo unaonetsedwa kwa ife.)+

  • Chivumbulutso 1:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 ndiponso wamoyo.+ Ndinali wakufa,+ koma taona, ndili ndi moyo kwamuyaya,+ ndipo ndili ndi makiyi a imfa+ ndi a Manda.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena