5Hiramu+ mfumu ya ku Turo+ inatumiza atumiki+ ake kwa Solomo, pakuti inamva kuti iyeyo ndi amene anadzozedwa kulowa ufumu m’malo mwa bambo ake, popeza Hiramuyo ankamukonda Davide masiku ake onse.+
11 Mfumu Solomo anapatsa Hiramu mizinda 20 m’dera la Galileya.+ (Hiramu+ mfumu ya Turo anathandiza Solomo+ ndi matabwa a mkungudza, matabwa a mitengo yofanana ndi mkungudza, ndi golide yense amene anafuna.)+
14Ndiyeno Hiramu+ mfumu ya Turo+ anatumiza amithenga kwa Davide. Anatumizanso matabwa a mkungudza,+ anthu omanga makoma, ndi anthu a ntchito zamatabwa kuti akamangire Davide nyumba.+