Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 5:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Hiramu+ mfumu ya ku Turo+ inatumiza atumiki+ ake kwa Solomo, pakuti inamva kuti iyeyo ndi amene anadzozedwa kulowa ufumu m’malo mwa bambo ake, popeza Hiramuyo ankamukonda Davide masiku ake onse.+

  • 1 Mafumu 9:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mfumu Solomo anapatsa Hiramu mizinda 20 m’dera la Galileya.+ (Hiramu+ mfumu ya Turo anathandiza Solomo+ ndi matabwa a mkungudza, matabwa a mitengo yofanana ndi mkungudza, ndi golide yense amene anafuna.)+

  • 1 Mbiri 14:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndiyeno Hiramu+ mfumu ya Turo+ anatumiza amithenga kwa Davide. Anatumizanso matabwa a mkungudza,+ anthu omanga makoma, ndi anthu a ntchito zamatabwa kuti akamangire Davide nyumba.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena