Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 5:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Hiramu+ mfumu ya ku Turo+ inatumiza atumiki+ ake kwa Solomo, pakuti inamva kuti iyeyo ndi amene anadzozedwa kulowa ufumu m’malo mwa bambo ake, popeza Hiramuyo ankamukonda Davide masiku ake onse.+

  • 1 Mafumu 5:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Hiramu+ atangomva mawu a Solomo, anasangalala kwambiri ndipo ananena kuti: “Yehova atamandike+ lero, popeza wapereka kwa Davide mwana wanzeru+ woti alamulire anthu ochulukawa.”+

  • 2 Mbiri 2:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndipo Solomo anatumiza uthenga kwa Hiramu+ mfumu ya Turo, kuti: “Monga momwe munachitira ndi Davide+ bambo anga pomawatumizira mitengo ya mkungudza kuti amangire nyumba yawo yokhalamo . . .

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena