Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 3:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Chotero iwo anamanga guwa lansembe lolimba pamalo ake+ akale, chifukwa anali kuopa anthu a mitundu ina.+ Atatero anayamba kuperekerapo nsembe zopsereza kwa Yehova, zam’mawa ndi zamadzulo.+

  • Nehemiya 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Onsewo anali kungofuna kutichititsa mantha, ndipo anali kunena kuti: “Manja awo+ adzalefuka ndipo adzasiya kugwira ntchitoyi, mwakuti siitha.” Inu Mulungu wanga, limbitsani manja anga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena