Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 M’chaka chachiwiri kuchokera pamene anabwera kunyumba ya Mulungu woona ku Yerusalemu, m’mwezi wachiwiri,+ Zerubabele+ mwana wa Salatiyeli,+ Yesuwa+ mwana wa Yehozadaki, abale awo onse, ansembe ndi Alevi, ndiponso anthu ena onse amene anabwera ku Yerusalemu kuchokera ku ukapolo,+ anayamba kugwira ntchitoyo. Kenako anaika Alevi+ m’malo awo kuyambira azaka 20 kupita m’tsogolo kuti akhale oyang’anira ntchito ya panyumba ya Yehova.+

  • Ezara 4:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma Zerubabele, Yesuwa,+ ndi atsogoleri ena onse+ a nyumba za makolo za Isiraeli anawayankha kuti: “Mulibe ufulu womanga nafe limodzi nyumba ya Mulungu wathu,+ pakuti ifeyo patokha timangira limodzi nyumba ya Yehova Mulungu wa Isiraeli, monga momwe Mfumu Koresi+ ya Perisiya yatilamulira.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena