Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 12:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Mwezi uno uzikhala mwezi wanu woyamba* wa miyezi ya pa chaka. Chaka chanu chiziyamba ndi mwezi uno.+

  • Levitiko 23:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 M’mwezi woyamba,* pa tsiku la 14 m’mweziwo,+ madzulo kuli kachisisira,* lizikhala tsiku la pasika+ wa Yehova.

  • Deuteronomo 16:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Muzisunga mwambo wa m’mwezi wa Abibu*+ pochita chikondwerero cha pasika kwa Yehova Mulungu wanu,+ chifukwa m’mwezi wa Abibu Yehova Mulungu wanu anakutulutsani mu Iguputo usiku.+

  • Esitere 3:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndiyeno m’mwezi woyamba,+ umene ndi mwezi wa Nisani,* m’chaka cha 12+ cha Mfumu Ahasiwero, munthu wina anachita Puri*+ kapena kuti Maere+ pamaso pa Hamani kuti adziwe tsiku ndi mwezi woyenerera. Choncho Maerewo anagwera mwezi wa 12 umene ndi mwezi wa Adara.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena