Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 4:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Eleazara mwana wa wansembe Aroni, aziyang’anira+ mafuta+ a nyale, zofukiza zonunkhira,+ nsembe yanthawi zonse yambewu,+ ndi mafuta odzozera.+ Aziyang’aniranso chihema chonse chopatulika ndi zonse za mmenemo, ndiwo malo oyerawo ndi ziwiya zake.”

  • 2 Mbiri 24:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Atangomaliza ntchitoyo anabweretsa ndalama zotsalazo kwa mfumu ndi Yehoyada. Ndi ndalamazo, iwo anapanga ziwiya za nyumba ya Yehova ndiponso ziwiya zogwiritsira ntchito pa utumiki+ ndi popereka zopereka. Anapanganso makapu+ ndi ziwiya zagolide+ ndi siliva, ndipo nsembe zopsereza+ zinayamba kuperekedwa nthawi zonse m’nyumba ya Yehova masiku onse a Yehoyada.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena