Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 2:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Usikuwo ndinatulukira pa Chipata cha Kuchigwa,+ kutsogolo kwa Kasupe wa Chinjoka Chachikulu* ndi kulowera ku Chipata cha Kumilu ya Phulusa.+ Pa nthawiyi, ndinali kuonetsetsa+ mmene mpanda wa Yerusalemu unawonongekera ndiponso mmene moto unawonongera zipata zake.+

  • Nehemiya 12:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Anadutsanso pamwamba pa Chipata cha Efuraimu,+ Chipata cha Mzinda Wakale,+ Chipata cha Nsomba+ mpaka kukafika pa Nsanja ya Hananeli,+ Nsanja ya Meya+ ndi ku Chipata cha Nkhosa,+ ndipo anaima pa Chipata cha Alonda.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena