Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ngati zingakukomereni mfumu, palembedwe makalata kuti anthu amenewa awonongedwe. Ine ndidzapereka matalente 10,000+ asiliva kwa anthu amene adzagwira ntchito imeneyi+ kuti abweretse matalentewo mosungiramo chuma cha mfumu.”

  • Esitere 4:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kenako Moredekai anauza Hataki zonse zimene zamuchitikira.+ Anamuuzanso zonse zokhudza ndalama zimene Hamani ananena kuti apereka mosungiramo chuma cha mfumu,+ n’cholinga chofuna kuwononga Ayuda.+

  • Esitere 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno anapatsa Hataki kalata+ imene munali lamulo lochokera ku Susani+ lakuti Ayuda afafanizidwe. Anamupatsa kalata imeneyi kuti akaonetse Esitere ndi kumuuza+ kuti akaonekere kwa mfumu ndi kuipempha kuti iwakomere mtima,+ ndiponso kuti Esitere akachonderere mfumu mwachindunji m’malo mwa anthu a mtundu wake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena