Genesis 6:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Ndiyeno ana a Mulungu+ woona anayamba kuona+ kuti ana aakazi a anthu anali okongola. Chotero, anayamba kudzitengera okha akazi alionse amene anawasankha. Deuteronomo 33:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Ndipo anati:“Yehova anafika kuchokera ku Sinai,+Anathwanima pa iwo kuchokera ku Seiri.+Anawala kuchokera kudera lamapiri la Parana,+Ndipo anali ndi miyandamiyanda ya oyera ake,+Kudzanja lake lamanja kunali ankhondo ake.+ Yobu 38:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Pamene nyenyezi za m’mawa+ zinafuula pamodzi mokondwera,Ndiponso pamene ana onse a Mulungu+ anayamba kufuula ndi chisangalalo? Danieli 3:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Ndiyeno mfumu inati: “Taonani! Inetu ndikuona amuna amphamvu anayi akuyendayenda pakati pa moto osapsa, ndipo munthu wachinayiyo akuoneka ngati mulungu.”+
2 Ndiyeno ana a Mulungu+ woona anayamba kuona+ kuti ana aakazi a anthu anali okongola. Chotero, anayamba kudzitengera okha akazi alionse amene anawasankha.
2 Ndipo anati:“Yehova anafika kuchokera ku Sinai,+Anathwanima pa iwo kuchokera ku Seiri.+Anawala kuchokera kudera lamapiri la Parana,+Ndipo anali ndi miyandamiyanda ya oyera ake,+Kudzanja lake lamanja kunali ankhondo ake.+
7 Pamene nyenyezi za m’mawa+ zinafuula pamodzi mokondwera,Ndiponso pamene ana onse a Mulungu+ anayamba kufuula ndi chisangalalo?
25 Ndiyeno mfumu inati: “Taonani! Inetu ndikuona amuna amphamvu anayi akuyendayenda pakati pa moto osapsa, ndipo munthu wachinayiyo akuoneka ngati mulungu.”+