Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 15:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndiyeno zimenezi zitachitika, Yehova analankhula ndi Abulamu m’masomphenya,+ kuti: “Usaope+ Abulamu. Ine ndine chishango chako.+ Mphoto yako idzakhala yaikulu kwambiri.”+

  • Genesis 31:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma bambo anu akhala akundipusitsa, ndipo asintha malipiro anga maulendo 10. Ngakhale ndi choncho, Mulungu sanawalole kuti andichite choipa.+

  • Deuteronomo 33:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Mulungu wakale lomwe ndiwo malo ako obisalamo,+

      Ndipo iwe uli m’manja amene adzakhalapo mpaka kalekale.+

      Adzapitikitsa mdani pamaso pako,+

      Ndipo adzanena kuti, ‘Awononge!’+

  • Salimo 34:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Mngelo wa Yehova amamanga msasa mozungulira onse oopa Mulungu,+

      Ndipo amawapulumutsa.+

  • Salimo 105:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mulungu sanalole kuti munthu aliyense awachitire zachinyengo,+

      Koma anadzudzula mafumu chifukwa cha iwo.+

  • 1 Petulo 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 inuyo amene Mulungu akukutetezani ndi mphamvu yake chifukwa muli ndi chikhulupiriro.+ Mulungu akukutetezani kuti mudzalandire chipulumutso,+ ndipo chipulumutso chimenechi chidzaonekera+ mu nthawi ya mapeto.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena