Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 38:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ndasokonezeka ndipo ndawerama kwambiri chifukwa cha chisoni changa.+

      Ndayenda uku ndi uku tsiku lonse ndili wachisoni.+

  • Salimo 42:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Ndidzauza Mulungu, thanthwe langa kuti:+

      “N’chifukwa chiyani mwandiiwala?+

      Ndikuyenderanji wachisoni chifukwa choponderezedwa ndi mdani wanga?”+

  • Salimo 43:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pakuti inu ndinu Mulungu wanga, ndinu malo anga achitetezo.+

      N’chifukwa chiyani mwanditaya?

      Ndikuyenderanji wachisoni chifukwa choponderezedwa ndi mdani wanga?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena