Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 38:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ndasokonezeka ndipo ndawerama kwambiri chifukwa cha chisoni changa.+

      Ndayenda uku ndi uku tsiku lonse ndili wachisoni.+

  • Salimo 43:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pakuti inu ndinu Mulungu wanga, ndinu malo anga achitetezo.+

      N’chifukwa chiyani mwanditaya?

      Ndikuyenderanji wachisoni chifukwa choponderezedwa ndi mdani wanga?+

  • Mlaliki 4:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ine ndinaganiziranso kuponderezana+ konse kumene kukuchitika padziko lapansi pano, ndipo ndinaona misozi ya anthu amene akuponderezedwa,+ koma panalibe wowatonthoza.+ M’manja mwa oponderezawo munali mphamvu, moti oponderezedwawo analibe wowatonthoza.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena