Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 31:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndamva zinthu zoipa zimene anthu ambiri akunena,+

      Ndamva zochititsa mantha kuchokera kumbali zonse.+

      Akasonkhana pamodzi kundichitira upo,+

      Amakonza chiwembu kuti achotse moyo wanga.+

  • Yeremiya 11:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndipo ine ndinali ngati mwana wa nkhosa wamphongo wokondedwa mwapadera, amene akupita kukaphedwa.+ Ine sindinadziwe kuti andikonzera ziwembu+ ndi kunena kuti: “Tiyeni tiwononge mtengowu pamodzi ndi zipatso zake. Tiyeni timuchotse m’dziko la anthu amoyo,+ kuti dzina lake lisakumbukikenso.”

  • Mateyu 12:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Afarisi atamva zimenezi ananena kuti: “Ameneyutu sikuti amatulutsa ziwanda ndi mphamvu zake ayi. Amatero ndi mphamvu ya Belezebule, wolamulira ziwanda.”+

  • 1 Petulo 2:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Iye sanachite tchimo,+ ndipo m’kamwa mwake simunapezeke chinyengo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena