Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 3:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Udzadya chakudya kuchokera m’thukuta la nkhope yako mpaka utabwerera kunthaka, pakuti n’kumene unatengedwa.+ Popeza ndiwe fumbi, kufumbiko udzabwerera.”+

  • Salimo 30:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Kodi magazi anga angakhale ndi phindu lanji ngati nditatsikira kudzenje la manda?+

      Kodi fumbi lidzakutamandani?+ Kodi lidzalengeza kuti inu ndinu woona?+

  • Salimo 88:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kodi anthu akufa mudzawachitira zodabwitsa?+

      Kapena kodi anthu akufa, anthu amene sangachite kanthu, adzauka?+

      Kodi adzakutamandani?+ [Seʹlah.]

  • Salimo 115:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Akufa satamanda Ya,+

      Ngakhalenso aliyense wotsikira kuli chete.+

  • Mlaliki 9:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pakuti amoyo amadziwa kuti adzafa,+ koma akufa sadziwa chilichonse.+ Iwo salandiranso malipiro alionse, chifukwa zonse zimene anthu akanawakumbukira nazo zaiwalika.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena