Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pamenepo mafumu a ku Edomu adzasokonezeka.

      Ndipo olamulira amphamvu a ku Mowabu adzanjenjemera ndi mantha.+

      Ndithu, anthu onse okhala mu Kanani adzataya mtima.+

  • Yesaya 13:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Anthu asokonezeka.+ Nsautso ndi zowawa za pobereka zawagwera. Iwo akumva zowawa ngati mkazi amene akubereka.+ Akuyang’anana modabwa. Nkhope zawo zafiira ndi mantha.+

  • Danieli 5:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Pa nthawi imeneyo nkhope ya mfumuyo inasintha ndipo inachita mantha.+ Miyendo yake inafooka+ ndipo mawondo ake anayamba kunjenjemera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena