Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 35:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iwo andikumbira mbuna popanda chifukwa ndi kuikapo ukonde,+

      Akumba mbunazo kuti ndigweremo ngakhale kuti sindinalakwe.+

  • Salimo 40:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Iye ananditulutsanso m’dzenje la madzi a mkokomo,+

      Ananditulutsa m’chithaphwi cha matope.+

      Kenako anapondetsa phazi langa pathanthwe.+

      Anandiyendetsa panthaka yolimba.+

  • Salimo 57:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Iwo anditchera ukonde panjira yanga.+

      Moyo wanga wagwidwa ndi chisoni.+

      Andikumbira mbuna.

      Koma iwo agweramo.+ [Seʹlah.]

  • Yeremiya 18:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kodi zabwino amazibwezera ndi zoipa?+ Kumbukirani nthawi zonse zija pamene ndinaima pamaso panu kuwalankhulira zabwino kuti muwachotsere mkwiyo wanu.+ Koma iwo tsopano andikumbira mbuna.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena