Deuteronomo 33:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Iye analinso kukonda anthu ake.+Oyera awo onse ali m’manja mwanu.+Iwowa anakhala pansi, pamapazi panu.+Anayamba kulandira ena mwa mawu anu.+ 2 Mbiri 29:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Tsopano mfumu Hezekiya+ inadzuka m’mawa kwambiri+ n’kusonkhanitsa akalonga+ a mzindawo, n’kupita kunyumba ya Yehova. Salimo 14:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Haa! Zikanakhala bwino m’Ziyoni mukanapezeka chipulumutso cha Isiraeli.+Yehova akadzasonkhanitsa ndi kubwezeretsa anthu ake amene anagwidwa ndi kutengedwa kupita kudziko lina,+Yakobo adzasangalale, Isiraeli adzakondwere.+ Miyambo 2:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 mwa kuyang’anitsitsa njira zachiweruzo,+ ndipo adzateteza njira ya anthu ake okhulupirika.+ Yesaya 13:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ine ndapereka lamulo kwa opatulika anga.+ Ndaitananso anthu anga amphamvu oti asonyeze mkwiyo wanga.+ Amenewa ndi anthu anga okondwa kwambiri.
3 Iye analinso kukonda anthu ake.+Oyera awo onse ali m’manja mwanu.+Iwowa anakhala pansi, pamapazi panu.+Anayamba kulandira ena mwa mawu anu.+
20 Tsopano mfumu Hezekiya+ inadzuka m’mawa kwambiri+ n’kusonkhanitsa akalonga+ a mzindawo, n’kupita kunyumba ya Yehova.
7 Haa! Zikanakhala bwino m’Ziyoni mukanapezeka chipulumutso cha Isiraeli.+Yehova akadzasonkhanitsa ndi kubwezeretsa anthu ake amene anagwidwa ndi kutengedwa kupita kudziko lina,+Yakobo adzasangalale, Isiraeli adzakondwere.+
3 Ine ndapereka lamulo kwa opatulika anga.+ Ndaitananso anthu anga amphamvu oti asonyeze mkwiyo wanga.+ Amenewa ndi anthu anga okondwa kwambiri.