Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 50:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Walekerera pakamwa pako kulankhula zinthu zoipa,+

      Ndipo ukugwiritsa ntchito lilime lako kulankhula zachinyengo.+

  • Salimo 57:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Moyo wanga uli pakati pa mikango.+

      Sindingachitire mwina koma kugona pakati pa ana a anthu, amene ali ngati nyama zoopsa zodya anthu,

      Amene mano awo ali ngati mikondo ndi mivi,+

      Ndipo lilime lawo lili ngati lupanga lakuthwa.+

  • Salimo 59:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Taonani! Amabwetuka ndi pakamwa pawo.+

      Milomo yawo ili ngati malupanga,+

      Pakuti iwo amati: “Ndani akumvetsera?”+

  • Salimo 64:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Amene anola lilime lawo ngati lupanga,+

      Amene alunjikitsa mivi yawo, imene ndi mawu awo owawa,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena