Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 22:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Agalu andizungulira.+

      Khamu la anthu ochita zoipa landizinga.+

      Iwo akuluma manja ndi mapazi anga ngati mkango.+

  • Salimo 59:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pakuti, taonani! Iwo akundidikirira kuti awononge moyo wanga.+

      Inu Yehova, anthu amphamvu akundiukira,+

      Ngakhale kuti ine sindinapanduke kapena kuchita tchimo lililonse.+

  • Salimo 86:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Inu Mulungu, anthu odzitukumula andiukira.+

      Khamu la anthu opondereza anzawo likufunafuna moyo wanga,+

      Ndipo sanakuikeni patsogolo pawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena