Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 52:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Olungama adzaona zimenezi ndi kuchita mantha,+

      Ndipo adzamuseka.+

  • Salimo 64:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Wolungama adzakondwera mwa Yehova ndipo adzathawira kwa iye,+

      Ndipo onse owongoka mtima adzatamanda Mulungu.+

  • Salimo 107:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Olungama amaona ndi kukondwera.+

      Koma anthu onse osalungama amatseka pakamwa.+

  • Ezekieli 25:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Anthu amenewa ndidzawalanga kwambiri ndi kuwadzudzula mwaukali,+ ndipo ndikadzawalanga adzadziwa kuti ine ndine Yehova.”’”+

  • Chivumbulutso 18:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 “Kondwerani kumwambako+ chifukwa cha zimene zamuchitikira. Inunso oyera,+ inu atumwi,+ ndi inu aneneri, kondwerani chifukwa Mulungu wamuweruza ndi kumupatsa chilango chifukwa cha zomwe anakuchitirani.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena