Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 32:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Inu olungama, kondwerani chifukwa cha zimene Yehova wachita ndipo sangalalani.+

      Fuulani ndi chisangalalo inu nonse owongoka mtima.+

  • Salimo 58:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Wolungama adzasangalala chifukwa chakuti waona oipa akupatsidwa chilango.+

      Adzasambitsa mapazi ake m’magazi a anthu oipa.+

  • Salimo 68:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Koma olungama asangalale,+

      Asekerere pamaso pa Mulungu,+

      Ndipo akondwere ndi kusangalala.+

  • Afilipi 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Nthawi zonse kondwerani mwa Ambuye.+ Ndibwerezanso, Kondwerani.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena