Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 5:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Imvani kufuula kwanga kopempha thandizo,+

      Inu Mfumu yanga+ ndi Mulungu wanga, chifukwa ndimapemphera kwa inu.+

  • Salimo 28:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Imvani mawu anga ochonderera pamene ndikufuulira inu kuti mundithandize,

      Pamene ndikukweza manja anga,+ nditayang’ana kumene kuli chipinda chamkati cha m’malo anu opatulika.+

  • Salimo 102:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 102 Inu Yehova, imvani pemphero langa.+

      Imvani kufuula kwanga kopempha thandizo.+

  • Salimo 130:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Imvani mawu anga Yehova.+

      Makutu anu amve mawu anga ochonderera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena