Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 6:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 “Tsopano Mulungu wanga, chonde, maso anu aone,+ ndipo makutu anu+ akhale tcheru kumvetsera pemphero lokhudza malo ano.

  • Salimo 17:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Imvani dandaulo lolungama, inu Yehova. Mvetserani kulira kwanga kochonderera.+

      Tcherani khutu ku pemphero langa limene likutuluka pamilomo yopanda chinyengo.+

  • Salimo 18:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Pa nthawi ya zowawa zanga ndinaitana Yehova,

      Ndinafuulira Mulungu wanga kuti andithandize.+

      Iye anamva mawu anga ali m’kachisi wake.+

      Pamenepo makutu ake anamva kulira kwanga kopempha thandizo.+

  • Salimo 34:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Maso a Yehova ali pa olungama,+

      Ndipo makutu ake amamva kufuula kwawo kopempha thandizo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena