Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Yehova adzamva ndithu pempho langa loti andikomere mtima.+

      Yehova adzalandira pemphero langa.+

  • Salimo 34:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Wosautsikayu anaitana ndipo Yehova anamva.+

      Anamupulumutsa m’masautso ake onse.+

  • Salimo 65:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Inu Wakumva pemphero, anthu a mitundu yonse adzabwera kwa inu.+

  • Salimo 116:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 116 Mtima wanga ndi wodzaza ndi chikondi, chifukwa Yehova amamva+

      Mawu anga ndi madandaulo anga.+

  • Maliro 3:56
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 56 Mumve mawu anga.+ Musatseke khutu lanu pamene ndikupempha mpumulo ndiponso pamene ndikulirira thandizo.+

  • 1 Yohane 3:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 ndipo chilichonse chimene tingapemphe, iye adzatipatsa,+ chifukwa tikusunga malamulo ake ndi kuchita zinthu zomukondweretsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena