Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 36:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Inu Mulungu, kukoma mtima kwanu kosatha ndi kwamtengo wapatali!+

      Ndipo ana a anthu amabisala mu mthunzi wa mapiko anu.+

  • Salimo 63:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pakuti kukoma mtima kwanu kosatha n’kwabwino kuposa moyo,+

      Milomo yanga idzakuyamikirani.+

  • Salimo 109:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Koma inu ndinu Yehova Ambuye Wamkulu Koposa.+

      Ndikomereni mtima chifukwa cha dzina lanu.+

      Ndilanditseni,+ popeza kukoma mtima kwanu kosatha ndi kwakukulu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena