Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 3:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ponena za moyo wanga, ambiri akuti:

      “Mulungu sam’pulumutsa ameneyu.”+ [Seʹlah.*]

  • Salimo 42:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Odana nane akunditonza kwambiri moti zikungokhala ngati mafupa anga aphwanyidwa,+

      Pakuti anthu akundifunsa tsiku lonse kuti: “Mulungu wako ali kuti?”+

  • Mateyu 27:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Suja amakhulupirira Mulungu? Mulunguyo am’pulumutse+ tsopano ngati akumufunadi. Ndi ujatu anali kunena kuti, ‘Ine ndine Mwana wa Mulungu.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena