Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 16:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Yehova wakubwezera mlandu wonse wa magazi a nyumba ya Sauli amene iwe unamulowa m’malo monga mfumu. Yehova wapereka ufumu m’manja mwa Abisalomu mwana wako. Ndipo tsopano tsoka lakugwera chifukwa uli ndi mlandu wamagazi!”+

  • Salimo 22:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Anthu onse ondiona amandinyodola.+

      Iwo amandinyogodola ndi pakamwa pawo, ndipo amapukusa mitu yawo mondinyoza.+ Iwo amati:

  • Mateyu 27:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Suja amakhulupirira Mulungu? Mulunguyo am’pulumutse+ tsopano ngati akumufunadi. Ndi ujatu anali kunena kuti, ‘Ine ndine Mwana wa Mulungu.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena