Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Inu Yehova, n’chifukwa chiyani adani anga achuluka chotere?+

      N’chifukwa chiyani anthu ondiukira achuluka?+

  • Salimo 3:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ponena za moyo wanga, ambiri akuti:

      “Mulungu sam’pulumutsa ameneyu.”+ [Seʹlah.*]

  • Salimo 7:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Inu Yehova Mulungu wanga,+ ine ndathawira kwa inu.+

      Ndipulumutseni kwa onse ondizunza ndipo mundilanditse,+

  • Salimo 71:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Iwo akunena kuti: “Mulungu wamusiya.+

      Mulondoleni ndi kumugwira pakuti palibe womulanditsa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena